The Ministry of Health has ramped up surveillance and public health measures to guard against the potential spread of Marburg…
Mavuto a zachuma akuchititsa anthu kuyika miyoyo yawo pa chiswe
Mavuto a zachuma akupangitsa anthu ochuluka kuyika miyoyo yawo pa chiswe pomwe akumalora kugwira nyansi ndi manja awo pofuna kupeza…
Anthu ena ku Balaka akufuna bwanamkubwa achoke
Mzika zokhudzidwa zochokera m’mudzi mwa Ng’onga mfumu yayikulu Nsamala m’boma la Balaka, zakonza ziwonetsero za bata zomwe cholinga chake ndikukakamiza…
CDEDI lati lipoti la ngozi ya ndege liperekedwe kwa a Malawi
Bungwe la Center for Democracy and Economic Development Initiative (CDEDI) lati likufuna kuti zikalata za lipoti lokhudza za ngozi ya…
CDEDI yati ikukonza ziwonetsero zosakondwa ndi boma
Bungwe la Centre for Democracy and Economic Development Initiatives (CDEDI), lati lachinayi likudzali lichititsa ziwonetsero mu nzinda wa Lilongwe zosonyeza…
CDEDI yati kalembera wa chisankho aime kaye
Bungwe la Centre for Democracy and Economic Initiatives (CDEDI) lapempha bungwe la Malawi Electoral Commission (MEC) kuti lisayambe gawo lachiwiri…
TB remains a challenge in Malawi – MLW
Malawi Liverpool Wellcome Programme (MLW) says tuberculosis (TB) remains a huge challenge which is pausing health risk to many lives.…
UDF sinalowe mu mgwirizano ndi chipani chilichonse
Mtsogoleri wa chipani cha United Democratic Front (UDF), Atupele Muluzi, watsimikizira akuluakulu a chipanichi kuti palibe chipani chilichonse chomwe akukambirana…
Chakwera wakhazikitsa komiti yapadera yoti ifufuze za ngozi ya ndege
Mtsogoleri wa dziko lino a Lazarus Chakwera wakhazikitsa komiti yapadera yoti ifufuze zokhudza ngozi ya ndege yomwe inapha wachiwiri kwa…
Govt commits to improving teachers’ welfare
Government has reaffirmed its commitment to evaluating teachers’ voices in policymaking and education reform, and to improving their working conditions.…
Bungwe la MEC lati zipani zisade nkhawa
Bungwe la Malawi Electoral Commission (MEC) latsutsa nkhawa za zipani zotsutsa m’dziko muno kuti bungweri liribe kuthekera koyendetsa chisankho cha…
Boma ladandaula ndi kuchepa kwa chidwi cha olemba ntchito
Unduna wa za umoyo wadandawula kaamba kakuchepa kwa chidwi chomwe anthu olemba anzawo ntchito akumayika pofuna kuti anthu awo adzikhala…