Mzika zokhudzidwa zochokera m’mudzi mwa Ng’onga mfumu yayikulu Nsamala m’boma la Balaka, zakonza ziwonetsero za bata zomwe cholinga chake ndikukakamiza…
Mutharika akwiya ndi kumangidwa kwa mamembala a DPP
Mtsogoleri wa chipani cha Democratic Progressive (DPP) a Peter Mutharika ati ndi wokwiya ndi kumangidwa kwa posachedwapa kwa akuluakulu a…
CDEDI lati lipoti la ngozi ya ndege liperekedwe kwa a Malawi
Bungwe la Center for Democracy and Economic Development Initiative (CDEDI) lati likufuna kuti zikalata za lipoti lokhudza za ngozi ya…
Chakwera walephera kulamulira dziko, watero Kabambe
Wolemba Lauryn M’banga Mtsogoleri wa chipani cha UTM a Dalitso Kabambe, ati mtsogoleri wa dziko lino a Lazarus Chakwera alephera…
CSAT yati iyamba kuphunzitsa anthu zokhudza nyumba ya malamulo
Bungwe la Centre for Social Accountability & Transparency (CSAT) lati kuyambira mwezi wa January chaka cha mawa lilimbikitsa ntchito yodziwitsa…
CDEDI yati ikukonza ziwonetsero zosakondwa ndi boma
Bungwe la Centre for Democracy and Economic Development Initiatives (CDEDI), lati lachinayi likudzali lichititsa ziwonetsero mu nzinda wa Lilongwe zosonyeza…
Nthambi ya ndende ilimbikitsa ntchito za manja
Nthambi ya ndende m’dziko muno yati kuphunzitsa anthu omwe akugwira ukaidi luso la ntchito za manja ndi njira imodzi yomwe…
Mkumano usonkhanitsa achinyamata 500 — NYCOM
Bungwe la National Youth Council of Malawi (NYCOM) lati zonse zokhudza mkumano wawukulu wa achinyamata mdziko muno omwe uyambe lolemba…
CDEDI yati kalembera wa chisankho aime kaye
Bungwe la Centre for Democracy and Economic Initiatives (CDEDI) lapempha bungwe la Malawi Electoral Commission (MEC) kuti lisayambe gawo lachiwiri…
Boma ladzipereka pofuna kuthetsa njala
Nduna yowona za malimidwe a Sam Kawale yati boma ladzipereka pofuna kuthetsa njala mdziko muno pogwiritsa ntchito ulimi wothilira. Iwo…
UDF sinalowe mu mgwirizano ndi chipani chilichonse
Mtsogoleri wa chipani cha United Democratic Front (UDF), Atupele Muluzi, watsimikizira akuluakulu a chipanichi kuti palibe chipani chilichonse chomwe akukambirana…
Chakwera wakhazikitsa komiti yapadera yoti ifufuze za ngozi ya ndege
Mtsogoleri wa dziko lino a Lazarus Chakwera wakhazikitsa komiti yapadera yoti ifufuze zokhudza ngozi ya ndege yomwe inapha wachiwiri kwa…